Thu Oct 07 2021 11:37:18 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
dc58078a40
commit
c5dee1897a
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 30 \v 31 Iwo ankayimiranso m'mawa uliwonse kuthokoza ndi kutamanda Yehova. Ankachitanso zimenezi madzulo ndi nthawi iliyonse yopereka nsembe zopsereza kwa Yehova, pa Sabata ndi pa zikondwerero za mwezi watsopano ndi masiku a maphwando. Chiwerengero chokhazikika, choperekedwa ndi lamulo, nthawi zonse chimayenera kupezeka pamaso pa Yehova.
|
||||
\v 30 Iwo ankayimiranso m'mawa uliwonse kuthokoza ndi kutamanda Yehova. Ankachitanso zimenezi madzulo \v 31 ndi nthawi iliyonse yopereka nsembe zopsereza kwa Yehova, pa Sabata ndi pa zikondwerero za mwezi watsopano ndi masiku a maphwando. Chiwerengero chokhazikika, choperekedwa ndi lamulo, nthawi zonse chimayenera kupezeka pamaso pa Yehova.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 32 Iwo anali kuyang'anira chihema chokumanako, malo oyera, ndipo anali kuthandiza abale awo a Aroni potumikira m'nyumba ya Yehova.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 24 \v 1 Magulu a anthu ogwira ntchito motsatira zidzukulu za Aaroni anali awa: \v 2 Nadabu, Abihu, Eleazara ndi Itamara. Nadabu ndi Abihu anamwalira abambo awo asanamwalire. Analibe ana, choncho Eleazara ndi Itamara anali ansembe. \v 3 Davide pamodzi ndi Zadoki, mbadwa ya Eleazara, ndi Ahimeleki, mbadwa ya Itamara, anawagawa m’magulu kuti azigwira ntchito yawo yaunsembe.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 24
|
|
@ -345,6 +345,10 @@
|
|||
"23-19",
|
||||
"23-21",
|
||||
"23-24",
|
||||
"23-27"
|
||||
"23-27",
|
||||
"23-30",
|
||||
"23-32",
|
||||
"24-title",
|
||||
"24-01"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue