Thu Oct 07 2021 11:53:28 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
6992f874e9
commit
66f12390ba
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 29 Kuchokera kwa Kisi: Mwana wa Kisi anali Yerameeli. \v 30 Ana a Musi anali Mali, Ederi, ndi Yerimoti. Awa anali Alevi potsata mabanja awo. \v 31 Amuna onse amene anali atsogoleri a nyumba ya makolo ndi aliyense wa abale awo achichepere anachita maere pamaso pa Mfumu Davide, Zadoki ndi Ahimeleki, pamodzi ndi atsogoleri a mabanja a ansembe ndi Alevi. Iwo anachita maere monga anachitira ana a Aroni.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 25 \v 1 Davide ndi atsogoleri a ankhondo anasankha ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni kuti alosere ndi zingwe ndi azeze ndi zinganga. Uwu ndiwo mndandanda wa amuna amene anatumikira: \v 2 Kuchokera mwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya, ndi Asharela, ana a Asafu motsogozedwa ndi Asafu amene anali kunenera motsogozedwa ndi mfumu. \v 3 Kuchokera mwa ana a Yedutuni: Gedaliya, Zeri, Yeshaya, Simeyi, Hasabiya, ndi Matitiya. Onse pamodzi analamulidwa ndi bambo awo Yedutuni, amene anali kuimba zeze posonyeza kuyamikira ndi kutamanda Yehova
|
|
@ -0,0 +1,2 @@
|
|||
Kuchokera mwa ana a Hemani panali Bukiya, Mataniya, Uziyeli,
|
||||
Shubaeli, Yerimoti, Hananiya, Hanani, Eliata, Gidalti, Romamti Ezeri, Yoshibekasha, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti. Onsewa anali ana a Hemani mneneri wa mfumu. Mulungu anapatsa Hemani ana khumi ndi anayi ndi ana aakazi atatu kuti akweze nyanga yake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 25
|
|
@ -358,6 +358,9 @@
|
|||
"24-19",
|
||||
"24-20",
|
||||
"24-23",
|
||||
"24-26"
|
||||
"24-26",
|
||||
"24-29",
|
||||
"25-title",
|
||||
"25-01"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue