Thu Oct 07 2021 11:29:18 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
646d4c4982
commit
56dbbf9aa4
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 17 \v 18 \v 19 Davide analamulanso atsogoleri onse a Israeli kuti athandize mwana wake Solomo. Tsopano funafunani Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse. dzina. "
|
||||
\v 17 Davide analamulanso atsogoleri onse a Israeli kuti athandize mwana wake Solomo. Tsopano funafunani Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse. dzina. nati, \v 18 "Yehova Mulungu wanu ali ndi inu, ndipo wakupatsani mtendere pozungulira ponse. Wapereka okhala m'manja mwanga m'manja mwanga. Dera lake lagonjetsedwa pamaso pa Yehova ndi anthu ake. \v 19 Tsopano funani Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse. Dzukani ndi kumanga malo opatulika a Yehova Mulungu. Mukatero mutha kubweretsa likasa la pangano la Yehova ndi zinthu za Mulungu, m'nyumba imene yamangidwa chifukwa cha dzina la Yehova. ""
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 23 \v 1 Davide atakalamba ndipo atatsala pang'ono kumwalira, analonga mwana wake Solomo kuti akhale mfumu ya Israeli. \v 2 Anasonkhanitsa atsogoleri onse a Israeli, pamodzi ndi ansembe ndi Alevi. \v 3 Anawerengedwa Alevi a zaka makumi atatu ndi kupitirirapo. Iwo analipo zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 23
|
|
@ -333,6 +333,9 @@
|
|||
"22-09",
|
||||
"22-11",
|
||||
"22-14",
|
||||
"22-15"
|
||||
"22-15",
|
||||
"22-17",
|
||||
"23-title",
|
||||
"23-01"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue