Thu Oct 07 2021 11:11:13 GMT+0200 (Central Africa Time)

This commit is contained in:
tsDesktop 2021-10-07 11:11:13 +02:00
parent efbb83a46c
commit 3efa564c22
7 changed files with 12 additions and 1 deletions

1
19/18.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 18 Aaramu anathawa mu Israeli, ndipo Davide anapha Aaramu okwanira 7,000 okwanira magaleta ndi asilikali 40,000 oyenda pansi. Komanso anapha Sofaki, mtsogoleri wa gulu lankhondo. \v 19 Mafumu onse amene anali atumiki a Hadadezeri ataona kuti agonjetsedwa ndi Aisraeli, anachita mtendere ndi Davide ndipo anawatumikira. Kotero Aaramu sanathenso kuthandiza Aamoni.

1
20/01.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\c 20 \v 1 Ndipo kunali, nthawi yamasika, nthawi yomwe mafumu nthawi zambiri amapita kunkhondo, Yoabu anatsogolera ankhondo kunkhondo, naononga dziko la ana a Amoni. Anapita nalinga ku Raba. Davide anakhalabe ku Yerusalemu. Yowabu anaukira Raba ndipo anagonjetsa mzindawo.

1
20/02.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 2 Davide anatenga chisoti chachifumu cha mfumu yawo kumutu kwake, ndipo anapeza kuti chimalemera talente limodzi la golide, ndipo munali miyala yamtengo wapatali. Korona uja anaveka Davide mutu wake, ndipo anatulutsa zofunkha za mzindawo zochuluka zedi. \v 3 Anatulutsa anthu omwe anali mu mzindawu ndikuwakakamiza kugwira ntchito yocheka macheka ndi zokumbira zachitsulo ndi nkhwangwa. Davide analamula mizinda yonse ya ana a Amoni kuti igwire ntchitoyi. Kenako Davide ndi anthu onse anabwerera ku Yerusalemu.

1
20/04.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 4 Pambuyo pa izi, panachitika nkhondo ku Gezeri ndi Afilisti. Sibbekai Mhushati anapha Sipai, mmodzi mwa mbadwa za Arefai, ndipo Afilisiti anagonjetsedwa. \v 5 Kumeneko kunalinso nkhondo ina ndi Afilisiti ku Gobu, ndipo Elhanani mwana wa Yairi wa ku Betelehemu anapha Lami m'bale wake wa Goliati Mgiti, amene ndodo ya mkondo wake inali ngati mtanda wa owomba nsalu.

1
20/06.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 6 \v 7 \v 8 Panali nkhondo ina ku Gati komwe kunali munthu wamtali kwambiri amene anali ndi zala zisanu ndi chimodzi kudzanja lililonse ndi zala zisanu ndi chimodzi kuphazi lililonse. Iyenso anali mbadwa ya Arefai. Atanyoza gulu lankhondo la Israeli, Yehonadabu mwana wa Shimea, mchimwene wa David, adamupha. Amenewa anali mbadwa za Arefai a ku Gati, + ndipo anaphedwa ndi dzanja la Davide ndi gulu la asilikali ake.

1
20/title.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
Mutu 20

View File

@ -306,6 +306,11 @@
"19-10",
"19-12",
"19-14",
"19-16"
"19-16",
"19-18",
"20-title",
"20-01",
"20-02",
"20-04"
]
}