nya-x-nyanja_jos_text_reg/07/19.txt

1 line
540 B
Plaintext

\v 19 Pamenepo Yoswa anakamba kuli Achari, ''mwana wanga, kamba cazoona pamenso ya Yehova, mulungu wa Israeli, na kupeleka zokamba zako kwa yeve. Nibuze camene wacita, osanibisa ine.'' \v 20 Akani anayankha Yoswa, ''zoona, naci mwila Yehova, mulungu wa Israyeli. Izi niye zamene ninacita: \v 21 Pamene nina bona pakati ka votengewa covala cokongola ca ku Babiloni, masikelo yali thu handiledi ya siliva, na cikute ca golide kelemela masikelo fifite, ninavi khumbwa nakuvitenga. Nivobisiwa pansi pakati ka cihema, na siliva ili pansi pake.''