nya-x-nyanja_jos_text_reg/05/08.txt

1 line
235 B
Plaintext

\v 8 Pamene onse bana jubiwa, banasalila kwamene banali kugona paka bana pola. \v 9 Ndipo Yehova anakamba kuli Yoswa, ''Siku yalelo na cosapo manyazi ya Eigipito pali imwe, cifukwa chake, zina ya malo inaitaniwa Giligala kufika nalelo.