nya-x-nyanja_jos_text_reg/02/10.txt

1 line
403 B
Plaintext

\v 10 Tinamvela mwamene Yehova anayumisila manzi ya mu nyanja imwe pamene pamene munacoka ku Eigipito. Tinamvelanso vamene munacita kumafumu yabili yaku Amori kumbali ya Yolodani - sihoni na ogi - yamene munabonongelatu. \v 11 Mwamusanga pamene tinamvela mitima yathu yanasungunuka kunalibe na mphavu inasala muli ali bonse - popeza Yehova mulungu wanu, nimulungu wa mwamba kumwamba na paziko ya pansi.