nya-x-nyanja_jos_text_reg/02/06.txt

1 line
188 B
Plaintext

\v 6 Koma anabakwelesa pamwamba pamalata na kubabisa namitenga yamene anaika pamalata. \v 7 Ndipo bamuna anaba pepeka pa njira yopita ku Yolodani. Ciseko cinavalika pamene opepeka anacoka.