nyu_rev_text_reg/18/01.txt

1 line
535 B
Plaintext

\c 18 \v 1 Bzitamala ibzi ndidaona mnjero winango akubuluka kuchoka kudzaulu. Wakukhala na ulamuliro bukulu, apo dziko lapansi lidabvunikiwa na ulemerero bwache. \v 2 Iye adakuwa na mafala yamphamvu, kuti, ''Wagwa, wagwa Babulo mkulu! Wasanduka mwakukhala bziwanda, mwakukoyera mizimu yensene yakunyansa, na mwakukoyera mbalame zense zakunyansa. \v 3 Thangwe mitundu yense yamwa vinyu wachigololo chache. Mafumu yadziko lapansi yachita naye chigololo. Wakuchita malonda wapadziko adala na mphamvu ya njira yachigololo cha moyo wache.''