Sat Nov 04 2023 19:08:29 GMT+0200 (Central Africa Time)

This commit is contained in:
tsDesktop 2023-11-04 19:08:30 +02:00
parent 472364964c
commit 22cfa8c4d0
2 changed files with 2 additions and 2 deletions

View File

@ -1,2 +1,2 @@
\v 59 \v 60 \v 61 Tsapano mkulu wa ansembe na akulu wa kutonga milandu adanya
ng'ana umboni bwa kunama kuti anamizire Yesu pala kuti amuphe. Adabusaya umboni, ngakhale kuti mboni zizinji zakunama zikhadabwera pompale. Soma kinangoka mboni ziwiri zidabwera, ''Zichiti ''Munthu umweyu adati, ''Ningakwanise kupasula tchalitchi ya Mulunguyi ndichiimanga pomwe nsiku zitatu basi,'''
ng'ana umboni bwa kunama kuti anamizire Yesu pala kuti amuphe. Adabusaya umboni, ngakhale kuti mboni zizinji zakunama zikhadabwera pompale. Soma kinangoka mboni ziwiri zidabwera, ''Zichiti ''Munthu umweyu adati, ''Ningakwanise kugwesa tchalitchi ya Mulunguyi ndichiimanga pomwe nsiku zitatu basi,'''

View File

@ -1 +1 @@
\v 62 \v 63 \v 64 mkulu wa ansembe adamuka achiti kuna iye,''Ulibe cakutawira? Soma Yesu adakhala chete. Mkulu wa ansembe adati kuna iye, ''Ndikukulumbirisa iwe kuna Mulungu wa moy, tiuze kuti ndiwedi mkirisitu, Mwana wa Mulungu.'' Yesu adati kuna iye, ''Mwatenepoyo ndimwe. Soma ndikukuuzani kuti,kucoka lero ate mtsogolo mumdzaona mwana wa Mulungu kukhala ku boko lamadidi la mphamvu, na kubwera mmitambo ya ku dzaulu.''
\v 62 \v 63 \v 64 Mkulu wa ansembe adamuka achiti kuna iye,''Ulibe cakutawira? Soma Yesu adakhala chete. Mkulu wa ansembe adati kuna iye, ''Ndikukulumbirisa iwe kuna Mulungu wa moy, tiuze kuti ndiwedi mkirisitu, Mwana wa Mulungu.'' Yesu adati kuna iye, ''Mwatenepoyo ndimwe. Soma ndikukuuzani kuti,kucoka lero ate mtsogolo mumdzaona mwana wa Mulungu kukhala ku boko lamadidi la mphamvu, na kubwera mmitambo ya ku dzaulu.''