Sat Mar 16 2024 15:03:37 GMT+0200 (Central Africa Time)

This commit is contained in:
tsDesktop 2024-03-16 15:03:37 +02:00
parent b708eb859b
commit 2ea50cd025
3 changed files with 2 additions and 3 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\c 7 \v 1 Akhali Melikizedekiyu, mfumu ya ku Salemu, wansembe wa Mulungu Mkulukulu, omwe adagumana na Abulahamu akubwerera kucoka kukapha mafumu achimudalisa. \v 2 Kukhali kwa iye ndiko Abulahamu adapereka chachikhumi cha chirichense. Kuyamba, kuthumbudzula kwa dzina lache ni, ''Mfumu ya chilungamo''; soma pomwe ni ''Mfumu ya ku Salemu,'' ndiye kuti, ''mfumu ya mtendere.'' \v 3 Iye alibe baba, ngwakusaya mayi, wakusaya mawerengewe ya chibadwidwe chache, alibe chiyambi cha nsiku zache ayai chimaliziro cha moyo wache. Apo ambandendemera na Mwana wa Mulungu, anikhalabe wansembe kwakusaya kulekeza.
\c 7 \v 1 Akhali Melikizedekiyu, mfumu ya ku Salemu, wansembe wa Mulungu Mkulukulu, omwe adagumana na Abulahamu akubwerera kucoka kukapha mafumu achimudalisa. \v 2 Kukhali kwa iye ndiko Abulahamu adapereka chachikhumi cha chirichense. Kuyamba, kuthumbudzula kwa dzina lache ni, ''Mfumu ya chilungamo''; soma pomwe ni ''Mfumu ya ku Salemu,'' ndiye kuti, ''mfumu ya mtendere.'' \v 3 Iye alibe baba, ngwakusaya mayi, wakusaya mawerengewe ya chibadwidwe chache, alibe chiyambi cha nsiku zache ayai chimaliziro cha moyo wache. Apo ambandendemera na Mwana wa Mulungu, anikhala basi wansembe kwakusaya kulekeza.

View File

@ -1 +1 @@
\v 4 Onani makulidwe ya munthuyu ndimo yakhaliri omwe Abulahamu m'bereki mkulu adamupasa chachikhumi cha ndibzo adakatenga kunkhondo. \v 5 Wana wa Levi omwe ambatambira basa la kupereka nsembe ana chitongi malingana na mtemo kutambira chachikhumi kuchoka kuna wanthu, ndiye kuti, kuchoka kuna abale wao, napo kuti iwo, pomwe, ali mbumba pomwe yakuchoka kuna Abulahamu. \v 6 Soma Melekizedeki, omwe mawerengedwe yachibadidwe chache yalibe kuchokera kuna iwo, adatambira chachikhumi kuchoka kuna Abulahamu, achimudalisa, omwe akhanayo malonjezano.
\v 4 Onani makulidwe ya munthuyu ndimo yakhaliri omwe Abulahamu m'bereki mkulu adamupa chachikhumi cha ndibzo adakatenga kunkhondo. \v 5 Wana wa Levi omwe ambatambira basa la kupereka nsembe ana chitongi malingana na mtemo kutambira chachikhumi kuchoka kuna wanthu, ndiye kuti, kuchoka kuna abale wao, napo kuti iwo, pomwe, ali mbumba pomwe yakuchoka kuna Abulahamu. \v 6 Soma Melekizedeki, omwe mawerengedwe yachibadidwe chache yalibe kuchokera kuna iwo, adatambira chachikhumi kuchoka kuna Abulahamu, achimudalisa, omwe akhanayo malonjezano.

View File

@ -85,7 +85,6 @@
"06-19",
"07-title",
"07-01",
"07-04",
"07-07",
"07-11",
"07-13",