\v 20 Tsono ife tidasankhiwa ninga wakuyimirira wa Khilistu, ninga pomwe Mulungu ali kutidandaulira kudzera mwa ife. Tikuku nginginmizani imwe, m'malo mwa Khilistu: ''Yanjanani mwa Mulungu!'' \v 21 Iye adakonza iwo omwe alibe kudziwa tchimo na kuyezera tchimo kuna ife, m'malo mwache ife tinikhala wachilungamo mwa Mulungu yekha.